Dataset Viewer
Auto-converted to Parquet Duplicate
score
float32
1.04
1.25
Ganda
stringlengths
9
500
Chichewa
stringlengths
9
500
1.248814
Naye omu ku mmwe mulyolyomi."
Komabe mmodzi wa inu ndi mdierekezi."
1.248393
Kubanga, laba, ntonda eggulu eriggya n'ensi empya: so ebintu ebyasooka tebirijjukirwa so tebiriyingira mu mwoyo.
"Ndilenga kumwamba kwatsopano [boma latsopano la kumwamba] ndi dziko lapansi latsopano [mtundu wa anthu olungama watsopano] ndipo zinthu zakale sizidzakumbukika, pena kulowa mumtima.
1.247785
Olwo ne balaba omwana w'omuntu ng'ajjira mu bire, ng'alina obuyinza bungi n'ekitiibwa kinene.
Kenako adzaona Mwana wa munthu akubwera mumtambo ndi mphamvu ndi ulemerero waukulu."
1.247496
Olwo ne balaba omwana w'omuntu ng'ajjira mu bire, ng'alina obuyinza bungi n'ekitiibwa kinene.
Ndipo adzaona Mwana wa munthu alimkudza mu mtambo ndi mphamvu ndi ulemerero waukulu ."
1.247292
Essanyu ery'emirembe n'emirembe liriba nga ngule ku mitwe gyabwe.
Ndipo wosatha chimwemwe kudzakhala pa mitu yawo.
1.247056
Obujulizi bwabwe (bwe bepampalika okuwa) bujja kuwandiikibwa era bagenda kubuuzibwa.
Umboni wawo ulembedwa ndipo adzafunsidwa (pazimenezo)!
1.246818
Bazadde bange tebaagenda naye nze nnagenda.
Makolo anga sanapite koma ine ndinapita.
1.246566
kubanga ndabye byonna Labbaani by'akukolera.
Chifukwa ndaona zonse zimene Labani wachita kwa inu.
1.246111
Tewali Katonda yakolebwa okusooka nze,
Ine ndisanakhaleko kunalibe Mulungu amene anapangidwa."
1.245735
Mmutoraine kuba omuheereza wangye ow'omutaano.'
Ndam'sankha akhale mtumiki wanga wapadera.'
1.244183
tuli bantu be era endiga ez'omu ddundiro lye.
Ndife anthu ake ndi nkhosa za pabusa pake."
1.243893
Enkya bajja kumanya ani mulimba omwerazi.
"Mawa lino adzadziwa (tsiku lakuwatsikira chilango,) kuti ndiyani wabodza wodzitukumula (iwo kapena Swaleh).
1.243724
3611:36 nny 3Awo Abayudaaya ne bagamba nti, "Ng'abadde amwagala nnyo!"
11:36 Choncho, Ayuda anati, "Onani mmene anamkonda!"
1.243657
Nnyinza ntya okukuwaayo ggwe Isirayiri?
Kodi ndingakupereke bwanji iwe Israeli?
1.243458
abaweereza bange bajja kunywa,
atumiki anga adzamwa,
1.241969
Ekikompe Kitange ky'ampadde, siikinywe?"
Kodi Ine ndisamwere chikho chimene Atate andipatsa?"
1.241705
17 Ebyo Maliyamu bye yayogera.
17 Zimene Mariya ankalankhula.
1.24132
Olwo nno ndyoke mbalumbire ddala nga mbava mu maaso ne mabega waabwe ne ku ddyo waabwe ne kkono, era togenda kusanga abasinga obungi mu bo nga beebaza.
"Kenako ndidzawadzera (mbali ya) kutsogolo kwawo, m'mbuyo mwawo, kumbali yakumanja kwawo ndi kumanzere kwawo, mwakuti simudzapeza ambiri a iwo oyamika.
1.241127
Kyandibadde kirungi singa omuntu oyo teyazaalirwa ddala."
Zikanakhala bwino munthu ameneyu akanapanda kubadwa."
1.240273
(Abantu abo) tebagenda kubeera na kya kulya kyonna okugyako e miti egy'amaggwa.
Ndipo alibe chakudya kupatula Mafinya (a anthu akumoto)
1.240199
'Abatuukirivu' abanaazuukizibwa be baani?
Kodi mbani 'anyakulungama' omwe an'dzalamusidwa?
1.240158
"Emirembe gibe mu ggulu, n'ekitiibwa kibeere waggulu ennyo!"
"Mtendere kumwamba ndi ulemerero mmwambamwamba!"
1.239594
Ne tuzimba waggulu wa mmwe emyaliiro emigumu musanvu.
Ndipo tamanga pamwamba panu thambo Zisanu ndi ziwiri zolimba;
1.239398
Mazima bombi ba mu baddu baffe abakkiriza (abannamaddala).
Ndithu, iye adali mmodzi mwa akapolo athu okhulupirira.
1.239206
Muwulirize mmwe amawanga gonna,
Imvani inu anthu a mitundu yonse;
1.238829
Omulumenhu oo a twikululwa okwa nyamukula a ti: "Omufimanekwa, Omona womunhu olyelye opo ndi mu itavele?"
Munthuyo anayankha kuti: "Kodi mwana wa munthuyo ndani ndimudziwe bambo, kuti ndikhulupirire mwa iye?"
1.238691
Kyandibadde kirungi singa omuntu oyo teyazaalirwa ddala."
Kukanakhala bwino kwa iye akanapanda kubadwa."
1.238456
Kiki nnabbi eyava mu Yuda ky'ataakola, era kiki ekyavaamu?
Kodi mneneri wa ku Yuda analephera kuchita chiyani, nanga zotsatira zake zinali zotani?
1.238293
Yokaana ajja kuba nnabbi, era ajja kuteekerateekera Masiya ekkubo.'
Juwau an'dzakhala mpolofeta, ndipo iye an'dzakonzera njira Mesiya.'
1.238263
17 Pi meno, medde ki lweny ki tekki ducu.
17 Tenepo pitirizani kumenya nkhondo.
1.237883
Nebagamba nti tukkirizza Mukama Katonda omulabirizi w'ebitonde.
"Adati: "Takhulupirira Mbuye wa zolengedwa zonse."
1.237228
"Ebintu ebingi [omuntu] by'aba nabyo si bye bimuwa obulamu."
Baibulo limanena kuti moyo wa munthu "suchokera m'zinthu zimene ali nazo."
1.236475
Atanjagala, ebigambo byange tabikwata.
Amene sandikonda ine sasunga mawu anga."
1.236172
n'awa abantu ebirabo."
ndipo anapereka mphatso kwa anthu."
1.235276
Kale Katonda wammwe alibawonya atya mu mukono gwange?' "
Ndipo mulungu amene adzakulanditsani m'manja mwanga ndani?'
1.235015
N'ayogera nti, "Abantu badduse mu lutalo, era bangi ku bo bafudde.
"Ndipo iye anati: "Anthu athawa kunkhondo, ndipo anthu ambiri agwa nafa.
1.23462
"Pe dong gibimedde ki pwonyo lweny"
"Anthuwo sadzaphunziranso nkhondo"
1.234576
Baba obaddeki Navio, Zamba ki temusiima?
Kodi bwanji sathokoza (Allah)?
1.234336
nnaamukuumanga, kubanga amanyi erinnya lyange.
Ndidzamuteteza chifukwa wadziwa dzina langa.
1.23429
Abaana baabwe balikiraba ne basanyuka,
Ana awo adzaziona zimenezi ndipo adzasangalala;
1.234273
38 Weena orikuunyikiriza, emigyera y'amaizi g'amagara eryahimintika neeruga omunda ye, nk'oku Ebyahandiikirwe birikugira.
Wokhulupirira mwa ine, monga Lemba limati, kutuluka m'kati mwake idzasonkhana wa madzi amoyo.
1.234223
'Nkusaba otugezese okumala ennaku 10,' bw'atyo bw'amugamba.
'Chonde tiyeseni kwa masiku 10,' akutero.
1.233581
Nga mugamba nti, 'Buli akola ebintu ebibi mulungi mu maaso ga Yakuwa, era amusanyukira,'+ oba nti, 'Katonda omwenkanya ali ludda wa?'"
Mwamutopetsa ponena kuti, "Aliyense amene amachita zoyipa ndi wabwino pamaso pa Yehova ndipo iye amakondwera naye" kapena pofunsa kuti, "Ali kuti Mulungu woweruza mwachilungamo?"
1.233574
2Yaabagira ati: Hakaba hariho omuramuzi omu kirorero kimwe, owaabaire atatiina Ruhanga, nobu kwakuba okweta aha muntu.
Iye anati, "Mʼmudzi wina munali woweruza wosaopa Mulungu ngakhalenso kulabadira za anthu.
1.233318
Ndimuwonya era ndimuwa ekitiibwa.
ndidzamupulumutsa ndi kumulemekeza.
1.233077
Emaali yaabwe n'abaana baabwe tebigenda kubagasa naakamu mumaaso g'a Katonda.
"Chuma chawo, ngakhale ana awo, sizidzawathandiza konse ku chilango cha Allah.
1.232621
Nagira ati, "Omwoyo w'amazima ku ariija aryabeebembera omu mazima goona."
Koma iyeyo akadzafika, mzimu wa choonadi, adzakutsogolerani m'choonadi chonse."
1.23235
Ebibala byagwo (okumanya bibi) biringa emitwe gya Sitane.
"Zipatso zake (nzoipa) ngati mitu ya asatana.
1.232245
Olina emikwano gy'abasajja emeka ku facebook?
Kodi muli ndi abwenzi angati pa Facebook?.
1.232103
(a) Abaruumi 8:30 egamba " era be yayawula edda, abo era yabayita: era be yayita, yabawa abo era obutuukirivu: era be yawa obutuukirivu, yabawa abo era ekitiibwa."
Rom 8:30 Ndipo amene Iye adawalamuliratuwo, Iye adawayitana ndipo iwo amene adawayitana adawalungamitsa,ndipo iwo amene adawalungamitsa adawapatsanso ulemerero.
1.231897
Bwatyo Katonda bw'abannyonnyola e bigambobye, musobole okubeera abeebaza.
Motero ndi momwe Allah akukufotokozerani zizindikiro Zake kuti muthokoze.
1.231469
Ono anaayitibwanga Mukazi,
Ameneyutu adzatchedwa Mkazi,
1.230187
Ng'ekyokulabirako, nnatandika okuyiga Olungereza.
Mwachitsanzo, ndinaganiza zophunzira Chingelezi.
1.229681
Timanyeti gose eriogo erio ndiabwatete abaibi abwo.
""Sindimadziwa chilichonse za akuluakulu a pamwamba (angelo) pamene amakangana (za kulengedwa kwa Adam)."
1.229408
Oba abaffe bo baaliwo nga tutonda ba Malayika nga bakazi.
"Kapena kuti tidalenga angelo kukhala akazi, iwo akuona?
1.228862
"Tebaliyingira mu kiwummulo kyange" (11)
"Iwowa sadzalowa ku malo anga a mpumulo."
1.22861
Ŋŋenda kumukolera omuyambi.'" - LUB.
Ndidzamupangira mnzake womuthandiza."
1.228458
nzija kumwesiga era siritya;
mwa Mulungu ine ndimadaliramo; sindidzachita mantha.
1.228238
13Naye Yakobo n'amuddamu nti, "Mukama wange amanyi nti abaana banafu, era n'ebisibo biyonsa, era singa bitambuzibwa awatali busaasizi bijja kufa.
13 Koma Yakobo anati kwa iye, "Mbuye wanga, inu mudziwa kuti anawa ndi a nthete ndiponso ndiyenera kusamalira nkhosa ndi ngʼombe zimene zikuyamwitsa ana awo.
1.228014
Era nsobi ki gye nkukoze, n'ondeetera nze n'obwakabaka bwange ekibi ekinene ekyenkana awo?
Kodi ife ndakulakwirani, kotero kuti idzabweretsa waukulu tchimo pa ine ndi pa ufumu wanga?
1.22787
Kyo kituufu nti tusaaliddwa nnyo Ow'oluganda Pierce.
N'zoona kuti tidzamusowa M'bale Pierce.
1.22785
Nnali mu kkomera ne mujja okundaba."
Ndinali m'ndende koma inu munabwera kudzandiona."
1.227209
Lowooza ennaku zange n'okutegana kwange; Era onsonyiwe ebibi byange byonna.
Penyani mazunzo anga ndi zovuta zanga; ndipo khululukirani zolakwa zanga zonse."
1.226782
Kale Mukama, Omulamuzi, leero alamule wakati w'abaana ba Isirayiri n'abaana ba Amoni.' "
Ambuye akhale woweruza ndi muweruzi lero, pakati pa Israel ndi ana a Amoni. "
1.226267
Anga omuntu aligiraki kuchungura oburorabwe? 27Manyasi Omwana w'Omuntu alija n'abamalaikabe omu kitinwa nk'ekya Ishe, arongore buli omoi aha rw'ebyo yakozire.
Mwana wa Munthu adzabwera mu ulemerero wa Atate wake limodzi ndi angelo ake, ndipo pomwepo mphoto kwa munthu aliyense monga mwa ntchito zake.
1.226052
Era oyo eyatya okuyimirira mu kifo kya Mukama omulabirizi we alina e jjana bbiri.
"Koma amene waopa kuti adzaimitsidwa kwa Mbuye wake (pa nthawi ya chiweruziro), adzalandira minda iwiri (yaikulu yamtendere).
1.226006
Ekibuga nga tekyetaaga njuba newankubadde omwezi okukyakira, kubanga ekitiibwa kya Katonda kyekimulisa, n'ettabaaza yaakyo ye Mwana gw'endiga.
Ndipo 1 pamzinda sipafunika dzuwa, kapena mwezi wakuuwalira; pakuti ulemerero wa Mulungu uunikira umenewu, ndipo nyali yace ndiye Mwanawankhosa.
1.225806
Twala mukyala wo ne bawala bo ababiri muve wano!'
Tenga mkazi wako ndi ana ako akazi awiri nutuluke muno!'
1.22578
Ajja kuba musanyufu nnyo okukubaganya naawe ebirowoozo ku nsonga ng'ezo.
Adzasangalala kukambirana nanu nkhani zimenezi.
1.225411
Lwaki Katonda yeebasa Adamu otulo otungi?
N'chifukwa chiyani Mulungu anagonetsa Adamu tulo tatikulu?
1.2252
32 Ne bamubuulira ekigambo kya Mukama waffe ne bonna abaali mu nnyumba ye.
16:32 Ndipo iwo anayankhula Mawu a Ambuye kwa iye, limodzi ndi onse amene anali m'nyumba yake.
1.224927
Nzija kugenda mulabe nga sinnafa."
Ndipita ndikamuone ndisanafe."
1.224881
Okusinza kwe bansinza biragiro abantu bye baayigiriza."
Amandilambira Ine kwachabe ndi kuphunzitsa malamulo ndi malangizo a anthu.' "
1.224769
Teyali Adamu.
Sanali Adamu.
1.224562
ne Samwiri yali mu abo abaakoowoolanga erinnya lye;
Samueli anali pamodzi ndi iwo amene anayitana pa dzina lake;
1.224464
15Omwe omuribo ku yaareebire yaakira, yaagarukayo naasingiza Ruhanga n'eiraka rihango.
Mmodzi wa iwo ataona kuti wachiritsidwa, anabwerera, akutamanda Mulungu mokweza mawu.
1.223937
Aye ngi abungu kisàka kyaabyo kyooso kishima, dingi ayitaanyina kintu kyooso mwishina dyaakyo."
Ndi amene akutsogolera gulu lonse la nyenyezizo malinga ndi chiwerengero chake, ndipo amaziitana potchula iliyonse dzina lake."
1.223867
17 Pi meno, medde ki lweny ki tekki ducu.
17 Choncho pitirizani kumenya nkhondo yolimbana ndi zinthu zimene zingakusokonezeni.
1.223826
2Yaabagira ati: Hakaba hariho omuramuzi omu kirorero kimwe, owaabaire atatiina Ruhanga, nobu kwakuba okweta aha muntu.
Iye alonga: "Mu nzinda unango mukhali nyakutonga miseru m'bodzi wakuti nee akhagopa Mulungu, pontho nee akhalemedza anthu.
1.223745
Si Yerusaalemi?
Kodi si Yerusalemu?
1.223722
Kyo kituufu nti tewali n'omu ku ffe yali alabye Katonda oba eyali alabye ekintu kyonna nga kitondebwa.
N'zoona kuti palibe munthu amene anaonapo Mulungu kapena kuona zinthu zikulengedwa.
1.222455
4 Era ku lunaku olwo mulyogera nti,
4 Tsiku limenelo mudzati:
1.222437
Mukama omulabirizi waabwe naabatumira nti ddala tujja kuzikiriza abeeyisa obubi.
Koma Mbuye wawo (Allah) adawavumbulutsira uthenga (wakuti): "Ndithu tiwaononga ochita zoipa (osakhulupirira)."
1.222229
Atanjagala, ebigambo byange tabikwata.
Iye amene sandikonda Ine sasunga mawu anga.
1.221984
Nnamuddamu nti, "Sirina muntu gwe mmanyi China."
Ndinamuuza kuti: "Sindidziwa munthu aliyense ku China."
1.221515
42 Tebajjukira buyinza bwe;
42 Sanakumbukire mphamvu zake,
1.221444
"Nebwonobasabira okubasonyiwa emirundi ensanvu, katonda tagenda kubasonyiwa." ([12])
Ngakhale utawapemphera chikhululuko chochuluka kwabasi mokwanira makumi asanu ndi awiri (70) Allah sangawakhululukire.
1.221399
15 N'abagamba nti Mugende mu nsi zonna, mubuulire enjiri eri ebitonde byonna.
15Anati kwa iwo, "Pitani mʼdziko lonse lapansi ndipo mukalalikire Uthenga Wabwino kwa zolengedwa zonse.
1.221276
20 So sibasabira bano bokka, naye n'abo abanzikiriza olw'ekigambo kyabwe;
Natenepa Yezu aphembera 'tayu basi thangwi ya awa [ale akhali cifupi na iye], mbwenye ndisakuphembanimbo thangwi ya ale anafuna kundikhulupira kubulukira ku mafala awo.'
1.221218
13 Yogera nabo mu ngeri ey'obukkakkamu.
13 Tizilankhula nawo mofatsa.
1.221195
21 Ekitundu ekirifikkawo kirikomawo, ekirifikkawo ku Yakobo, eri Katonda ow'amaanyi.
Otsalira adzatembenuzira kumbuyo, otsalira a Yakobo, kwa Mulungu Wamphamvu.
1.22105
Abantu baafiirwa batya eddembe erya nnamaddala?
Kodi anthu anataya bwanji ufulu weniweni?
1.221024
Tolaba maanyi ga Katonda mu bintu ng'ebyo?
Kodi simuona mphamvu za Mulungu m'zinthu zimenezi?
1.221003
Sulemaani addamu: 'Yakuwa Katonda wange, nkyali muto era simanyi kufuga.
Solomo anayankha kuti: 'Yehova Mulungu wanga, ndiri wamng'ono ndipo sindidziwa kulamulira.
1.220842
(Abakkiriza), mwe mutiibwa mu mitima gyabwe okusinga bwe batya Katonda.
"Ndithu inu (Asilamu) mukuopedwa kwambiri m'mitima mwawo kuposa mmene akumuopera Allah.
1.220616
Naye kijja kitya okuba nti basobola okwogera ennimi zaffe?'
Ndiyeno zikutheka bwanji kuti azilankhula zilankhulo zathu?'
1.220358
Mu bigambo eby'obunnabbi, Maliyamu yeeyongera okutendereza Katonda, ng'agamba nti: "Akoze eby'amaanyi n'omukono gwe, asaasaanyizza abo abooleka amalala mu mitima gyabwe.
Mariya anapitiriza kulemekeza Mulungu ndipo ananena mawu omwe ndi ulosi kuti: "Wachita zamphamvu ndi dzanja lake, wabalalitsira kutali odzikweza m'zolinga za mitima yawo.
1.220065
Abaffe mmwe mwatandikawo omuti gwagwo, oba ffe twagutandika.
"Kodi ndinu amene mudameretsa mitengo yake kapena Ndife tidaipanga?
1.220045
Kino kyanakuwaza nnyo Lutti, kubanga yali musajja mulungi.
Pyenepi pyanensa Loti, thangwi iye akhali munthu wadidi.
1.220015
Mazima (Nuhu) ali mu baddu baffe abakkiriza aba nnamaddala.
Ndithu Iye adali m'modzi mwa akapolo athu okhulupilira.
End of preview. Expand in Data Studio

Ganda-Chichewa_Sentence-Pairs Dataset

This dataset contains sentence pairs for African languages along with similarity scores. It can be used for machine translation, sentence alignment, or other natural language processing tasks.

This dataset is based on the NLLBv1 dataset, published on OPUS under an open-source initiative led by META. You can find more information here: OPUS - NLLB-v1

Metadata

  • File Name: Ganda-Chichewa_Sentence-Pairs
  • Number of Rows: 187295
  • Number of Columns: 3
  • Columns: score, Ganda, Chichewa

Dataset Description

The dataset contains sentence pairs in African languages with an associated similarity score. Each row consists of three columns:

  1. score: The similarity score between the two sentences (range from 0 to 1).
  2. Ganda: The first sentence in the pair (language 1).
  3. Chichewa: The second sentence in the pair (language 2).

This dataset is intended for use in training and evaluating machine learning models for tasks like translation, sentence similarity, and cross-lingual transfer learning.

References

Below are papers related to how the data was collected and used in various multilingual and cross-lingual applications:

[1] Holger Schwenk and Matthijs Douze, Learning Joint Multilingual Sentence Representations with Neural Machine Translation, ACL workshop on Representation Learning for NLP, 2017

[2] Holger Schwenk and Xian Li, A Corpus for Multilingual Document Classification in Eight Languages, LREC, pages 3548-3551, 2018.

[3] Holger Schwenk, Filtering and Mining Parallel Data in a Joint Multilingual Space ACL, July 2018

[4] Alexis Conneau, Guillaume Lample, Ruty Rinott, Adina Williams, Samuel R. Bowman, Holger Schwenk and Veselin Stoyanov, XNLI: Cross-lingual Sentence Understanding through Inference, EMNLP, 2018.

[5] Mikel Artetxe and Holger Schwenk, Margin-based Parallel Corpus Mining with Multilingual Sentence Embeddings arXiv, Nov 3 2018.

[6] Mikel Artetxe and Holger Schwenk, Massively Multilingual Sentence Embeddings for Zero-Shot Cross-Lingual Transfer and Beyond arXiv, Dec 26 2018.

[7] Holger Schwenk, Vishrav Chaudhary, Shuo Sun, Hongyu Gong and Paco Guzman, WikiMatrix: Mining 135M Parallel Sentences in 1620 Language Pairs from Wikipedia arXiv, July 11 2019.

[8] Holger Schwenk, Guillaume Wenzek, Sergey Edunov, Edouard Grave and Armand Joulin CCMatrix: Mining Billions of High-Quality Parallel Sentences on the WEB

[9] Paul-Ambroise Duquenne, Hongyu Gong, Holger Schwenk, Multimodal and Multilingual Embeddings for Large-Scale Speech Mining, NeurIPS 2021, pages 15748-15761.

[10] Kevin Heffernan, Onur Celebi, and Holger Schwenk, Bitext Mining Using Distilled Sentence Representations for Low-Resource Languages

Downloads last month
6

Collection including michsethowusu/ganda-chichewa_sentence-pairs